by Admin | Mar 18, 2022 | Fasting, Fatawa, Featured, Fiqh, Islam
Kodi ndichiphunzitso cha Mtumiki kusala kwa tsiku la 15 Sha’baan? Hadith yomwe yabwera polimbikitsa swalaat ndi kusala komanso kuchita ibaada yosiyanasiyana pa 15 Sha’baan, siili mugulu la ma Hadith ofooka (a dhwaeef) koma ili mugulu la ma Hadith opeka komanso abodza...
by Admin | Feb 27, 2022 | Featured, Islam, Sunnah
Kodi n’chifukwa chani ma Sheikh amalalikira pamaliro ndi kumanda pomwe imfayo payokha ndi mlaliki? Tibwelere kaye mbuyo pang’ono, makamaka pa mawu oti: كَفَى بِالمَوْتِ وَاعِظًا “Yakwanira imfa kukhala mlaliki” Mawu amenewa ambiri amanena kuti ndi Hadith ya...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Islam, Misconceptions
Kuchokera mu Minhaajul Qaaswideen fi Fadhlil Khulafaai Rraashideen page 187, tidziwa kuti nawo ma Khawaarij amadana ndi ena mwa ma Swahaba. Khawaarij ndigulu la anthu omwe anali limodzi ndi Ali radhia Allah anhu pa nkhondo zake, koma anamutuluka ndikumuwukira pamene...
by Admin | Sep 4, 2021 | Fasting, Featured, Fiqh, Islam, Sunnah
Kuchokera m’mawu omwe anthu amati ndi ochokera kwa Mtumiki salla Allah alaih wasallam, عن أبي هريرة قال: قال رسول الله ﷺ : أول شهر رمضان رحمة، وأوسطه مغفرة، وآخره عتق من النار. منكر، روه الديلمي Nkhani inachokera kwa Abi Hurairah radhia Allah anhu, anati:...
by Admin | Sep 4, 2021 | Fatawa, Featured, Fiqh, Islam, Islamic Manners, Marriage, Misconceptions
خـــاتَمُ الخِـــطْبَةِ ENGAGEMENT (WEDDING) RING(Sheikh Naasiru Ddeen Al-Albaani) Kuyamikidwa konse nkwa Allah, Mbuye wa zolengedwa zonse, Mtendere ndi Madalitso zipite kwa uyo yemwe Allah anamutumiza kuti adzakwaniritse makhalidwe abwino. Pali zichitochito zina...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Islam, Misconceptions, Role Models
“Kodi ‘Uthman Radhia Allah Anhu Atamwalira Anaikidwa Kuti?” ‘Uthman radhia Allah anhu atamwalira anasambitsidwa ndi kuvekedwa, ndipo kenako ananyamulidwa ndigulu la antchito ake, ndipo anapempheretsa janaza yake Swahaba Jubayru bun Mut’im, ma...
Your Comments