by Admin | May 7, 2020 | Salaat, Sunnah
Allah Ta’la amayandikira (ndi ulemelero wake) usiku uliwonse pa thambo la dziko lapansi, ndipo amaitana: “kodi alipo yemwe akundipempha ndimuyankhe? nanga alipo yemwe akupempha chikhululuko ndimukhululukire? kodi alipo yemwe akufuna kulapa machimo ake...
by Admin | Feb 16, 2020 | Featured, Sunnah
Pali ma hadith omwe anapekedwa nalembedwa mu buku kuti tidziwerenga poikira umboni kuti kuwerenga Qur’an ku Manda ndi Sunnah. Ma hadith amenewa ndi osafunika kuti tidziwagwiritsa ntchito tikawaona. Chifukwa ndi ma hadith oipa omwe amanamizira Mtumiki salla Allah...
by Admin | Feb 11, 2020 | Featured, Fiqh, Sunnah
GAWO LACHIWIRI Imodzi mwa nkhani zovuta kudzimvesetsa chifukwa cha kuchepekedwa kwa maphunziroku ndi yomwe ndikufuna kulongosola lero…ndipo pankhaniyi ndakhala ndikuona ma sheikh omwe akhala akuyesetsa kuwalongosolera anthu, akunyozedwa poyankhuliridwa...
by Admin | Feb 11, 2020 | Featured, Fiqh, Sunnah
بسم الله الرحمن الرحيم الحمد لله رب العالمين والصلاة والسلام على رسوله الكريم وعلى آله وأصحابه ومن تبعهم إلى يوم الدين أما بعد Pali mitu yomwe imakambidwa ndi ma Sheikh, yomwe ndiyofunikira kwambiriimene munthu amati akangoyankhula, anthu omwe sazindikira –...
by Admin | Jun 20, 2019 | Sunnah
Mtumiki salla Allah alaih wasallam anayankhula zokhunza Black Seed (Njere Zakuda حبة سوداء) kuti ndi mankhwala a nthenda iliyonse kupatula imfa. Posachedwapa ma dokotala atulukira kuti ndizoonazdi Black Seed amachiza matenda osiyanasiyana, monga mtima ndi ena ambiri...
by Admin | Dec 2, 2018 | Sunnah
Mahr (Dowry) Islam has legislated the giving of the dower by the husband to the wife in order to please the woman’s heart and to honor her. It is also meant to bring an end to what was done in the Days of Ignorance wherein she was wronged, exploited, despised and...
Your Comments