by Admin | Jan 10, 2020 | Fatawa, Marriage
Liwu loti “Bridal” (bride to be) likuimira mkazi yemwe ali ndi ukwati wake posachedwa. “Shower” ndi kupereka mwambo ndi mphatso komanso madalitso ndi malangizo ndi kumukondwelera pamene azikakhala m’banja ndi mwamuna wake. Malingana ndi...
by Admin | Jan 10, 2020 | Fatawa, Marriage
Kusiyana kwa veil ndi wedding dress Ma Sheikh odalirika pamaphunziro a Chisilamu akhala akuchilimika kuletsa chovala chija chotchedwa “veil” pa nikaah. Lero tikufuna tichitirepo chidwi ndi kufotokoza momveka bwino pa nkhani imeneyi kuti aliyense atenge choonadi cha...
by Admin | Jan 10, 2020 | Fatawa, Marriage
Walimah ndi phwando kapena chisangalalo chomwe chimabwera kumapeto komangitsa banja (Nikaah). Ndizololedwa kuchita walimah nthawi yomweyo kapena kuchedwetsa malingana ndi kuthekera kwa munthu, ndipo iyenera kuchitika munjira yomwe ili yololedwa ndi malamulo a...
by Admin | Jan 10, 2020 | Fatawa, Marriage
Zomwe zimachitika masiku ano zobisa mahr nkudzaitanitsa nthawi yomwe nikaah ikuchitika, si chiphunzitso cha Chisilamu, komanso mboni ziwiri kufunsa mahr tsiku la nikaah sichiphunzitso cha Chisilamu. Mahr imayenera kukhala ikudziwika kwa waliyy (muyang’aniri wa mkazi)...
by Admin | Jan 10, 2020 | Fatawa, Marriage
Zofunika pa nthawi ya nikaah Pangani Download PDF yake Okwatira Pamene mwambo wa nikaah ukuchitikira malo aliwonse omwe anthu asankha (monga munsikiti, m’nyumba ngakhalenso mu office ya Sheikh), malo aliwonsewo omwe tikufuna kuchitiramo mwambo wa nikaah siziri...
by Admin | Jun 9, 2019 | Marriage
Qur’an Yolemekezeka yatchula munthu mmodzimmodzi momveka bwino, omwe omwe sali oyenera kumanga nawo banja. Anthu amenewa ndi awa: حُرِّمَتْ عَلَيْكُمْ أُمَّهَاتُكُمْ وَبَنَاتُكُمْ وَأَخَوَاتُكُمْ وَعَمَّاتُكُمْ وَخَالاَتُكُمْ وَبَنَاتُ الأَخِ وَبَنَاتُ الأُخْتِ...
Your Comments