by Admin | Jul 17, 2020 | Islam, Islamic Manners
Pali anthu ena anazolowera kulumbira m’Dzina la Allah, mwachitsanzo kunena kuti “Wallahi…”, ndipo amachitenga kukhala chizolowezi chawo pakuyankhula kulikonse, zofunikira ngakhale zosafunikira. Chizolowezi choterechi ndicholakwika kwambiri....
by Admin | Jul 2, 2019 | Islamic Manners
Panopa dziko likuyenda chonchi:Yemwe amatsata za dziko akutengedwa kuti ndi otsogola chifukwa zikubwera mwatsopano. Ndiye otereyo kalikonse ka mu deen akumakachita mwa fashion malinga ndi mmene dziko likuyendera. Yemwe amagwiritsa imaan yake molimba potsatira...
by Admin | Jun 19, 2019 | Islamic Manners
Kulibwino kumangomva mbiri ya Al Mu’ayidiyy, kusiyana ndikumuwona تسمع عن المعيدي خير من أن تراه Umenewu ndi mwambi wa kalekale pakati pa ma Arabs munthawi ya umbuli Mtumiki asanabadwe. Ndipo anayankhula Al Nu’man bun Al Mundhir (yemwe anali mfumu pa...
by Admin | May 15, 2019 | Islamic Manners
Kodi ndi njira yanji yomwe ophunzira angalangizire Sheikh wake? Zomwe zili zoyenera ndi opposite; Sheikh ndi yemwe akuyenera kulangiza ophunzira wake, chifukwa iyeyo ndi amene ali ozindikira zinthu komanso odziwa kuposa ophunzirayo. Ophunzira nthawi zonse amakhala...
by Admin | May 2, 2019 | Islamic Manners
Ma Ulamaa (anthu ozindikira komanso amaphunzitsa za deen ya Chisilamu), ndi anthu olemekezeka pamaso pa Allah chifukwa choti iwo ndi Alowammalo a Aneneri, ndi atsogoleri oyenera kuwalemekeza kuposa mtsogoleri wa dziko chifukwa akutitsogolera ku moyo wosatha....
by Admin | Oct 6, 2018 | Islamic Manners
“Ndi zoletsedwa mu Chisilamu mkazi kuvala buluku (thalauza) lothina ndikuonetsa mmene thupi lake liliri. Ndipo chilango chake ndi choopsa zedi chifukwa mchitidwe umenewu umafalitsa machimo pa dziko.” Darul Iftail Misriy Allah anaika ndondomeko ya momwe...
Your Comments