by Hamdan Zefa | Mar 4, 2022 | Featured, Fiqh, Marriage, Misconceptions, Sunnah
Bodza loyamba: “Akazi pa mitala amakhala m’nyumba imodzi” Anthu ena amaganiza kuti mitala ikutanthawuza kuti mwamuna atenge akazi awiri ndikumakhala nawo m’nyumba imodzi, komanso kuti mikangano imene ingakhalepo pakati pa akaziwa itha...
by Admin | Feb 27, 2022 | Featured, Islam, Sunnah
Kodi n’chifukwa chani ma Sheikh amalalikira pamaliro ndi kumanda pomwe imfayo payokha ndi mlaliki? Tibwelere kaye mbuyo pang’ono, makamaka pa mawu oti: كَفَى بِالمَوْتِ وَاعِظًا “Yakwanira imfa kukhala mlaliki” Mawu amenewa ambiri amanena kuti ndi Hadith ya...
by Admin | Sep 5, 2021 | Featured, Shia
HUSAIN .. MADAD YA HUSAIN .. YA HUSAIN !! Nchifukwa chani ma Shia amatamanda ndi kulemekeza Husain (رضي الله عنه) yekha ndi kusiya ana ena onse a Ali (رضي الله عنه)? Kodi munayamba mwadzifunsapo funso limeneli? Nanga nkhani imeneyi inayamba yakudabwitsanipo?...
by Admin | Sep 4, 2021 | Fasting, Fatawa, Featured, Fiqh
KUBWEZA (QADHAA) MASIKU OSIYIDWA PAKUSALA MWEZI WA RAMADHAN Qadhaa ya Swawm ndi chani? Qadhaa ya swawm ndiko kusala kwa munthu yemwe sanasale masiku ena a mwezi wa Ramadhan, kapena kumusalira m’bale wake pambuyo poti munthu wamwalira atasiya swawm yomwe analonjeza kwa...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Shia
KODI MA SHIATU RAAFIDA NDI ASILAMU OKHULUPILIRA?Pomwe iwo anapanga shahaada ndipo amaikira umboni kuti palibe wopembedzedwa mwachoonadi kupatula Allah, ndikuti Muhammad ndi Mtumiki wake, komanso Qibla yawo ndi ku Makkah ndipo amaswali munsikiti? Siyense yemwe wapanga...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Fiqh, Salaat
Kuchotsedwa Kwa Kuwerenga Pambuyo Pa Imaam Mu Swalaat/Rakaat Zokweza Mawu Swifatu Swalaat Nabiy salla Allah alaih wasallam (Sheikh Al Albaani) pge 98 Kodi Kuwerenga Surah Al Fatiha kunalolezedwa nthawi yanji nanga kunaletsedwa nthawi yanji? Mtumiki salla Allah alaih...
Your Comments