by Hamdan Zefa | May 22, 2022 | Featured, Shia
Kutamandidwa konse ndi kwa Allaah, Wapamwambamwamba, Yemwe alibe wothandizana naye mu Ufumu Wake, Yemwe ali m’Modzi, Yemwe ali Wakutha kuchita chili chonse ndipo kwa Iye ndi komwe kuli Chiongoko. Mtendere ndi madalitso zipite kwa Mtumiki Muhammad (ﷺ), aku banja ake...
by Hamdan Zefa | Mar 6, 2022 | Featured, Fiqh, Marriage, Misconceptions, Sunnah
Bodza lachinayi: “Mitala imachepetsa ma Rizq” Lina mwa maina a Allaah ndi Ar-Razzaaq (Wopereka ma Rizq). Tikamakamba za ma Rizq, tikukamba chirichonse chimene munthu amapeza pano pa dziko lapansi ndipo Mwini ma rizq amenewa ndi Allaah osati ife anthu....
by Hamdan Zefa | Mar 6, 2022 | Featured, Fiqh, Marriage, Misconceptions, Sunnah
Bodza lachitatu: “Mitala imayambitsa matenda” Nkhani ya mitala idazunguliridwa ndi zokamba zambiri zomwe sizili zolondola. Kwa ena mwa akazi amene mwamuna wawo wagwidwa akugonana ndi mkazi wina, iwo samakhumbanso kuti akhudzidwe (akhale limodzi ndi mwamuna...
by Hamdan Zefa | Mar 6, 2022 | Featured, Fiqh, Marriage, Misconceptions, Sunnah
Ibn Qudaamah mu Al-Mughniy, (vol. 8, tsamba 151) adati: وَقَدْ اشْتُهِرَ بينَ النَّاس وجودُ عَقْدِ الرَّجُلِ عن امرأتِه حينَ يَتزوَّجُها. فلا يَقْدِرُ على إتْيانِها، وحَلُّ عَقْدِه، فيَقْدِرُ عليها بعدَ عَجْزِه عنها، حتى صار مُتواتِرًا لا يُمْكِنُ جَحْدُه. ورُوِىَ من...
by Hamdan Zefa | Mar 5, 2022 | Featured, Fiqh, Marriage, Misconceptions, Sunnah
Bodza lachiwiri (2/1) “Mitala imayambitsa ufiti” Akazi ena amaopa kuvomera kukhala mkazi wachiwiri, wachitatu kapena wachinayi chifukwa choti adamva zoti mkazi woyamba amachita matsenga kapena ufiti kuti awapatse mavuto akazi amene mwamuna wake...
Your Comments