by Admin | Jul 17, 2020 | Featured, Islam
Tikudziwa bwinolomwe kuti ena mwa majinn ndi ma shaytwaan (asatana), amenewa ndi ma jinn oipa, ndipo asatanawa amafa mmene amafera majinn ndi anthu. Onsewa akulowa mukuyankhula kwa Allah Ta’ala koti: كُلُّ مَنْ عَلَيْهَا فَانٍ – وَيَبْقَى وَجْهُ رَبِّكَ...
by Admin | Jul 12, 2020 | Featured, Prophets
Akazi a Mtumiki Muhammad salla Allahu alaih wasallam 1. Khadeejah bint Khuwaylid 2. Saudah bint Zam’ah 3. Aaishah bin Abi Bakr Al Siddiq 4. Hafswahbint Umar bun Al Khatwaab 5. Zainab bint Khuzaymah 6. Umm Salamah (Hind bint Abi Umayyah) 7. Zainab bint Jahsh 8....
by Admin | Jun 10, 2020 | Featured, Islam
KUCHOTSA KUSAMVETSETSA PA MA HADITH OMWE ABWERA KUTI “MLIRI SUDZALOWA MU MZINDA WA MADINAH” (Abu Shareef C Idris) Download PDF>> الحمد لله، القائل ﴿ أَحَسِبَ النَّاسُ أَنْ يُتْرَكُوا أَنْ يَقُولُوا آمَنَّا وَهُمْ لَا يُفْتَنُونَ ﴾ وقال ﴿...
by Admin | May 6, 2020 | Fasting, Featured, Fiqh
Anzathu ena ambiri akamapanga wudhu sachukucha mkamwa akuti kuwopa kuwononga swaum yawo. Zimenezitu ndizolakwika pazifukwa zambiri: 1. Kuchukucha mkamwa sikuwononga swaum ngati ukupanga wudhu, ngakhale madzi atalowa kukhosi mwangozi swaum yako sinawonongeke. 2. Palibe...
by Admin | Feb 17, 2020 | Featured, Fiqh, Islam
Imeneyi ndi swalaat yomwe imapempheredwa dera lina lotalikira komwe swalat Janaza yachitikira. Maswalidwe a swalaatul ghaaib ndichimodzimodzi swalaatul janaaza. Komatu swalat imeneyi (swalaatul ghaaib) ili ndi malamulo osiyana ndi swalaatul janaza makamaka pa munthu...
by Admin | Feb 16, 2020 | Featured, Islam
Funso: Kodi nchifukwa chani anthu amakonda kufunsa kuti “ndikufunafuna Sheikh omwe amachotsa ziwanda, amene ali ndi number yawo anditumizire?” Yankho: Amafuna kuti akawawelengere Qur’an, ma Dua ndi ma Dhikr chifukwa iwowo sadziwa, komanso safuna...
Your Comments