by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Fiqh, Salaat
Kuchotsedwa Kwa Kuwerenga Pambuyo Pa Imaam Mu Swalaat/Rakaat Zokweza Mawu Swifatu Swalaat Nabiy salla Allah alaih wasallam (Sheikh Al Albaani) pge 98 Kodi Kuwerenga Surah Al Fatiha kunalolezedwa nthawi yanji nanga kunaletsedwa nthawi yanji? Mtumiki salla Allah alaih...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Islam, Prophets, Salaat
Ndizofunika Kwa Msilamu Aliyense Kudziwa Kusiyana Kwa Masjidul Aqsa Ndi Masjid Qubbat Assakharah. Kuyambira kalekale kwambiri, Masjidul Aqsa ku Palestine yakhala ikukumana ndi zipsinjo zambiri kuchokera kwa adani a Chisilamu omwe safuna kuona Chisilamu chikufalikira...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Fiqh, Misconceptions, Salaat
Taraweh ndi swalaat yausiku yomwe timaswali mmwezi wa Ramadhan, pokwaniritsa Sunnah ya Mtumiki salla Allah laaih wasallam yomwe sanali kuisiya. Ndipo swalaat imeneyi imatheka kuswalidwa pa jamaah kapena pawekha kunyumba, monganso mmene Mtumiki anali kuchitira....
by Admin | Sep 3, 2021 | Fiqh, Islam, Misconceptions, Salaat
Anthu ambiri akamaliza swalah za faradh ndikumaliza kupanga ma Adhikaar, amanyamula manja awo ndikuyamba kupanga Dua pagulu kapena payekhapayekha aliyense. Ndipo pali gulu la anthu ena omwe samapanga, koma amati akamaliza kupanga ma adhkaar basi amatuluka, poti ma dua...
by Admin | Dec 10, 2020 | Fatawa, Featured, Fiqh, Salaat
KODI NDIZOLOLEDWA KUMASULIRA KHUTBAH YA JUM’AH MUCHIYANKHULO CHINA ZITAKHALA KUTI ANTHU OMVETSERA SAKUVA CHIARABU? Nkhaniyi anthu amasiyana zokamba zenizeni chifukwa choti nthawi ya Mtumiki kunalibe kumasulira, komanso panalibe chifukwa chomasulira khutbah poti...
by Ahmad Lasimu | Jul 12, 2020 | Fiqh, Salaat
Awa ndimalo omwe ali oletsedwa kupangiramo swalaat 1. Ku Manda Mtumiki Muhammad salla Allah alaih wasallam ananena mu Hadith kuti: لعن الله اليهود والنصارى اتخذوا قبور أنبيائهم مساجد Allah adawatembelera Ayuda ndi Akhristu kamba koti adatenga manda azineneri awo...
Your Comments