by Admin | May 24, 2022 | Featured, Islam, Prophets
A TURNING POINT IN THE HISTORY OF ISLAM. Abdulkarim Shuaib May 20, 2022 02:56AM (Source: Book of Seerah ibn Hisham and Arab news 2012 religion article) The incident of Hudaibiyah reserves in history a significant phase of Islam when Muslims got an opportunity to...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Islam, Prophets, Salaat
Ndizofunika Kwa Msilamu Aliyense Kudziwa Kusiyana Kwa Masjidul Aqsa Ndi Masjid Qubbat Assakharah. Kuyambira kalekale kwambiri, Masjidul Aqsa ku Palestine yakhala ikukumana ndi zipsinjo zambiri kuchokera kwa adani a Chisilamu omwe safuna kuona Chisilamu chikufalikira...
by Admin | Jul 12, 2020 | Featured, Prophets
Akazi a Mtumiki Muhammad salla Allahu alaih wasallam 1. Khadeejah bint Khuwaylid 2. Saudah bint Zam’ah 3. Aaishah bin Abi Bakr Al Siddiq 4. Hafswahbint Umar bun Al Khatwaab 5. Zainab bint Khuzaymah 6. Umm Salamah (Hind bint Abi Umayyah) 7. Zainab bint Jahsh 8....
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Uzair anali munthu woyera komanso wanzeru. Anakhala pambuyo pa Mneneri Sulaiman alaih salaam komanso asanabwere Mneneri Zakaria alaih salaam. Tsiku lina monga mwachizolowezi chake, Mneneri anakayendera munda wake pa bulu. Chakumasana, anafika pa kamzinda kena...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Ma ulamaa akuluakulu amakhulupilira kuti Shuaib alaih salaam anali munthu wachikulire yemwe anateteza Musa alaih salaam. Mneneri Musa alaih salaam anakwatira mwana wa Mneneri Shuaib alaih salaam asanapite ku Egypt. Koma palibe maumboni ovomereza kapena kutsutsa...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Yusha alaih salaam anali chidzukulu chachikulu cha Mneneri Musa alaih salaam. Anali ndi agogo akewo pa ulendo waukulu wochokera mu Egypt. Musa alaih salaam anali kumkonda mzukulu wakeyu kotero anampatsa ntchito zofunikira zambiri. Anayenda mu chipululu kwa zaka...
Your Comments