by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Islam, Prophets, Salaat
Ndizofunika Kwa Msilamu Aliyense Kudziwa Kusiyana Kwa Masjidul Aqsa Ndi Masjid Qubbat Assakharah. Kuyambira kalekale kwambiri, Masjidul Aqsa ku Palestine yakhala ikukumana ndi zipsinjo zambiri kuchokera kwa adani a Chisilamu omwe safuna kuona Chisilamu chikufalikira...
by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Fiqh, Misconceptions, Salaat
Taraweh ndi swalaat yausiku yomwe timaswali mmwezi wa Ramadhan, pokwaniritsa Sunnah ya Mtumiki salla Allah laaih wasallam yomwe sanali kuisiya. Ndipo swalaat imeneyi imatheka kuswalidwa pa jamaah kapena pawekha kunyumba, monganso mmene Mtumiki anali kuchitira....
by Admin | Sep 3, 2021 | Fiqh, Islam, Misconceptions, Salaat
Anthu ambiri akamaliza swalah za faradh ndikumaliza kupanga ma Adhikaar, amanyamula manja awo ndikuyamba kupanga Dua pagulu kapena payekhapayekha aliyense. Ndipo pali gulu la anthu ena omwe samapanga, koma amati akamaliza kupanga ma adhkaar basi amatuluka, poti ma dua...
by Admin | Sep 3, 2021 | Featured, Fiqh, Misconceptions
Kuyamikidwa konse nkwa Allah, Yemwe ananena kuti: Watukuka ndi kudalitsika (Allah) Amene m’manja Mwake muli ufumu (wochita chilichonse pazolengedwa zonse); ndipo Iye ali ndi mphamvu yokwanira pachilichonse. Amene adalenga imfa ndi moyo kuti akuyeseni (mayeso) ndani...
by Admin | Apr 8, 2021 | Fasting, Featured, Fiqh
Kuyambikidwa konse nkwa Allah Mwini zolengedwa zonse, Mtendere ndi Madalitso zipite kwa Mtumiki wake wolemekezeka. Kodi tikhonzekere motani mwezi wa Ramadhan? Pamene tili pa chitseko cha mwezi wa Ramadhan, aliyense mwa ife akuyenera kuti akudziwa komwe akupita...
by Admin | Apr 7, 2021 | Featured, Fiqh, Marriage
Mitala mu Chisilamu si LAMULO LOKAKAMIZIDWA, koma ndi chilolezo kwa yemwe wafuna. Allah Ta’la analoleza mitala mu Surat Al Nisaai Aayah #3. Nkhani ya mitala imavuta mbali zonse; kwa mwamuna ndi kwa mkazi komwe, chifukwa cha kusatsatira ndondomeko komanso...
Your Comments