by Admin | Sep 3, 2021 | Featured, Fiqh, Misconceptions
Kuyamikidwa konse nkwa Allah, Yemwe ananena kuti: Watukuka ndi kudalitsika (Allah) Amene m’manja Mwake muli ufumu (wochita chilichonse pazolengedwa zonse); ndipo Iye ali ndi mphamvu yokwanira pachilichonse. Amene adalenga imfa ndi moyo kuti akuyeseni (mayeso) ndani...
by Admin | Sep 3, 2021 | Featured, Misconceptions
KUCHOTSA CHIKAIKO PA KUSOKONEKERA KWA ANTHU ENA PA MATANTHAUZO A ENA MWA MA AAYAH A MU QUR’AN YOLEMEKEZEKASurah Ad Dhuha (Aayah #7) وَوَجَدَكَ ضَالًّا فَهَدَى – الضحى 7 “Ndipo adakupeza uli wosazindikira (Qur’an) nakuongola (pokuzindikiritsa Qur’aniyo ndi malamulo a...
by Admin | Apr 8, 2021 | Fasting, Featured, Fiqh
Kuyambikidwa konse nkwa Allah Mwini zolengedwa zonse, Mtendere ndi Madalitso zipite kwa Mtumiki wake wolemekezeka. Kodi tikhonzekere motani mwezi wa Ramadhan? Pamene tili pa chitseko cha mwezi wa Ramadhan, aliyense mwa ife akuyenera kuti akudziwa komwe akupita...
by Admin | Apr 7, 2021 | Featured, Fiqh, Marriage
Mitala mu Chisilamu si LAMULO LOKAKAMIZIDWA, koma ndi chilolezo kwa yemwe wafuna. Allah Ta’la analoleza mitala mu Surat Al Nisaai Aayah #3. Nkhani ya mitala imavuta mbali zonse; kwa mwamuna ndi kwa mkazi komwe, chifukwa cha kusatsatira ndondomeko komanso...
by Admin | Apr 6, 2021 | Fatawa, Featured, Islamic Manners
Basharul Haafi rahimahu Allah anati: “Yemwe amakonda kuti azifunsidwa (za deen), sali oyenera kufunsidwa” قال بشر الحافي رحمه الله تعالى: مَن أحبَّ أن يُسْأَلَ، فَليسَ بِأَهْلٍ لِأَنْ يُسْألَ. Mau awa ndi akuya zedi. Allah atipatse kumvesetsa Phunziro:...
by Admin | Mar 31, 2021 | Featured, Islam, Misconceptions
The Position of Islam and Muslims on GOOD FRIDAY AND EASTER (Holidays 2nd & 5th April, 2021) For those who love Isa (Jesus) son of Mary ‘Alaihima Ssalaam GOOD FRIDAY is a Christian holiday commemorating the ostensible crucifixion of Jesus and his death at...
Your Comments