by Admin | Feb 16, 2020 | Featured, Sunnah
Pali ma hadith omwe anapekedwa nalembedwa mu buku kuti tidziwerenga poikira umboni kuti kuwerenga Qur’an ku Manda ndi Sunnah. Ma hadith amenewa ndi osafunika kuti tidziwagwiritsa ntchito tikawaona. Chifukwa ndi ma hadith oipa omwe amanamizira Mtumiki salla Allah...
by Admin | Feb 11, 2020 | Featured, Fiqh, Sunnah
GAWO LACHIWIRI Imodzi mwa nkhani zovuta kudzimvesetsa chifukwa cha kuchepekedwa kwa maphunziroku ndi yomwe ndikufuna kulongosola lero…ndipo pankhaniyi ndakhala ndikuona ma sheikh omwe akhala akuyesetsa kuwalongosolera anthu, akunyozedwa poyankhuliridwa...
by Admin | Feb 11, 2020 | Featured, Fiqh, Sunnah
بسم الله الرحمن الرحيم الحمد لله رب العالمين والصلاة والسلام على رسوله الكريم وعلى آله وأصحابه ومن تبعهم إلى يوم الدين أما بعد Pali mitu yomwe imakambidwa ndi ma Sheikh, yomwe ndiyofunikira kwambiriimene munthu amati akangoyankhula, anthu omwe sazindikira –...
by Admin | Nov 11, 2019 | Featured, Salaat
Tiyeni titsegule page103 ya chitabu cha أحكام الجنائز وبدعها cha Allaamatu Sheikh Muhammad Naasirul-Deen Al Albaaniy, ndipo tiyambire pa mutu wa number 13 kumapita kutsogolo mmapage otsatira mu chitabuchi Zoyenera kuchita pa Janaaza Janaaza ndi mwambo wa maliro womwe...
by Admin | Nov 4, 2019 | Fatawa, Featured
Fodya ndi chimodzi mwa zinthu zomwe zangobwera posachedwapa ndipo mbuyomu kunalibe. Nthawi ya Mtumiki salla Allah alaih wasallam kunalibe kugwiritsa ntchito fodya, komanso mbuyo mwakemo nthawi ya Atumiki onse kunalibe. Nthawi ya ma Shawabanso kunalibe fodya,...
by Admin | Aug 7, 2019 | Featured
Pambuyo pa kuwerenga zolembedwa zoyambilira zokhunza amayi, anthu omwe sali Asilamu akhonza kukhala ndi funso lofanana loti: Kodi akazi a Chisilamu lero lino akutengedwa malinga momwe zalembedwera mu bukumu? Yankho lake ndiloti: Ayi. Kopa popeza funso ili sililephera...
Your Comments