Yakwanira Imfa Kukhala Mlaliki

Kodi n’chifukwa chani ma Sheikh amalalikira pamaliro ndi kumanda pomwe imfayo payokha ndi mlaliki? Tibwelere kaye mbuyo pang’ono, makamaka pa mawu oti: كَفَى بِالمَوْتِ وَاعِظًا “Yakwanira imfa kukhala mlaliki” Mawu amenewa ambiri amanena kuti ndi Hadith ya...

Ahlu Bayt…

HUSAIN .. MADAD YA HUSAIN .. YA HUSAIN !! Nchifukwa chani ma Shia amatamanda ndi kulemekeza Husain (رضي الله عنه) yekha ndi kusiya ana ena onse a Ali (رضي الله عنه)? Kodi munayamba mwadzifunsapo funso limeneli? Nanga nkhani imeneyi inayamba yakudabwitsanipo?...

Zofunika kwa Azimai ndi Atsikana – Swawm

KUBWEZA (QADHAA) MASIKU OSIYIDWA PAKUSALA MWEZI WA RAMADHAN Qadhaa ya Swawm ndi chani? Qadhaa ya swawm ndiko kusala kwa munthu yemwe sanasale masiku ena a mwezi wa Ramadhan, kapena kumusalira m’bale wake pambuyo poti munthu wamwalira atasiya swawm yomwe analonjeza kwa...