Du’a Pambuyo pa Swalaat za Faradh

Anthu ambiri akamaliza swalah za faradh ndikumaliza kupanga ma Adhikaar, amanyamula manja awo ndikuyamba kupanga Dua pagulu kapena payekhapayekha aliyense. Ndipo pali gulu la anthu ena omwe samapanga, koma amati akamaliza kupanga ma adhkaar basi amatuluka, poti ma dua...

“Hijaamah” Ndichiyani?

Hijaama ndi liwu la Chiarabu lomwe likutanthauza muchiyankhulocho kuti “kuyamwa”, monga mmene timayankhulira kuti “mwana akuyamwa bere la mai ake” حجم الطفل ثدي أمه أو مص الطفل ثدي أمه Tsopano liwu loti حجم Likutanthauza size, ndipo likugwiritsidwa ntchito chifukwa...

Kukhonzekera Mwezi wa Ramadhan

Kuyambikidwa konse nkwa Allah Mwini zolengedwa zonse, Mtendere ndi Madalitso zipite kwa Mtumiki wake wolemekezeka. Kodi tikhonzekere motani mwezi wa Ramadhan? Pamene tili pa chitseko cha mwezi wa Ramadhan, aliyense mwa ife akuyenera kuti akudziwa komwe akupita...