Kodi ma Shia ndiAsilamu?

KODI MA SHIATU RAAFIDA NDI ASILAMU OKHULUPILIRA?Pomwe iwo anapanga shahaada ndipo amaikira umboni kuti palibe wopembedzedwa mwachoonadi kupatula Allah, ndikuti Muhammad ndi Mtumiki wake, komanso Qibla yawo ndi ku Makkah ndipo amaswali munsikiti? Siyense yemwe wapanga...

Kuwerenga Pambuyo pa Imaam

Kuchotsedwa Kwa Kuwerenga Pambuyo Pa Imaam Mu Swalaat/Rakaat Zokweza Mawu Swifatu Swalaat Nabiy salla Allah alaih wasallam (Sheikh Al Albaani) pge 98 Kodi Kuwerenga Surah Al Fatiha kunalolezedwa nthawi yanji nanga kunaletsedwa nthawi yanji? Mtumiki salla Allah alaih...

Kugawidwa Patatu kwa Mwezi wa Ramadhan

Kuchokera m’mawu omwe anthu amati ndi ochokera kwa Mtumiki salla Allah alaih wasallam, عن أبي هريرة قال: قال رسول الله ﷺ : أول شهر رمضان رحمة، وأوسطه مغفرة، وآخره عتق من النار. منكر، روه الديلمي Nkhani inachokera kwa Abi Hurairah radhia Allah anhu, anati:...