Zakaat ndi Chani

Zakaat ndi Chani

Kuyamikidwa ndi kwa Allah ndipo mtendere ndi madalitso zikhale pa Mtumiki wathu Muhammad salla Allah alaih wasallam,,,amma ba’d Mukuona kwanga ndapeza kuti chiwelengero cha Asilamu ambiri sakumapereka Zakaat kuno ku Malawi. Ndipo izi sichifukwa choti anthuwo...

Nthawi za Mapemphero

Ambiri masiku ano amasokonezeka nthawi ya swalat yomwe anaphunzitsa Mtumiki salla Alaih waallam, ndi  wotchi makamaka akapita dziko lina. Ena anati “mzikiti womwe timaswali kuno ndi wa Mashia chifukwa akumachita adhaan ya Dhuhr past 1, pomwe ku Malawi...
Ulowammalo Pa Chuma Chotsala

Ulowammalo Pa Chuma Chotsala

بسم الله الرحمن الرحيم Kugawa Chuma Chosiyidwa Malinga ndi Qur’an Yolemekezeka Munthu akamwalira nkusiya chuma, Asilamu akuyemera kugawa chumacho moyenera ndi abale ake omwe wasiya omwalirayo. Nzomvetsa chisoni masiku ano munthu ali ndi makolo ake, azibale ake,...
Zofunika kwa Ophunzira

Zofunika kwa Ophunzira

Zinthu Zofunikira Kuti Yemwe Akufuna Kuphunzira Ayambilire Kuchita Kuti Adziteteze Phunziro limeneli likuchokera pa mutu woti “Ahlu Ssunnati wa ‘alaamaatihim” Sheikh Rabieu bun Haadi Al Madkhali Kufunafuna maphunziro mu deen ndi lamulo kwa wina...
Ma Imaam Anayi

Ma Imaam Anayi

Tiwadziwe ma Imaam a Madh’hab Anayi 1. Imaam Abu Hanifa AlNu’man bun Thabit 2. Imaam Maalik bun Anas 3. Imaam Muhammad bun Idris AlShaafi’iy 4. Imaam Ahmad bun Hanbal Anthu amene amatsatira Qur’an ndi Sunnah za Mtumiki salla Allah alaih...
Malovu a Galu

Malovu a Galu

Ndi chifukwa chani timayenera kutsuka ndi mchenga kamodzi? “Kuyeretsa kwa chiwiya chanu chomwe wanyambitamo galu ndi kutsuka ka 7, kamodzi kakeko ndi mchenga”. Tonse tikudziwa kuti Mtumiki anatiuza kuti tidzitsuka chiwiya chomwe galu wanyambita ka seven,...