by Admin | Feb 11, 2020 | Featured, Fiqh, Sunnah
بسم الله الرحمن الرحيم الحمد لله رب العالمين والصلاة والسلام على رسوله الكريم وعلى آله وأصحابه ومن تبعهم إلى يوم الدين أما بعد Pali mitu yomwe imakambidwa ndi ma Sheikh, yomwe ndiyofunikira kwambiriimene munthu amati akangoyankhula, anthu omwe sazindikira –...
by Admin | Jun 20, 2019 | Sunnah
Mtumiki salla Allah alaih wasallam anayankhula zokhunza Black Seed (Njere Zakuda حبة سوداء) kuti ndi mankhwala a nthenda iliyonse kupatula imfa. Posachedwapa ma dokotala atulukira kuti ndizoonazdi Black Seed amachiza matenda osiyanasiyana, monga mtima ndi ena ambiri...
by Admin | Dec 2, 2018 | Sunnah
Mahr (Dowry) Islam has legislated the giving of the dower by the husband to the wife in order to please the woman’s heart and to honor her. It is also meant to bring an end to what was done in the Days of Ignorance wherein she was wronged, exploited, despised and...
by Admin | Nov 11, 2018 | Sunnah
الحمد لله رب العالمين، والصلاة والسلام على رسوله الكريم وبعد Kuyamikidwa konse ndi kwa Mbuye wa zolengedwa zonse, yomwe anatipanga ife kukhala Asilamu nachipanga Chisilamu kukhala Chipembedzo chokhacho chomwe chidzalandiridwe pamaso pake. Akunena mu Surah Aali Imraan...
by Admin | Nov 8, 2018 | Sunnah
KODI PALI DUA YOPEZERA MWAMUNA/MKAZI WABANJA? Tidziwe kaye kuti dua ndi chani. Imeneyi ndi ibaadah komanso njira imodzi yodziyandikitsira kwa Allah chifukwa munthu umadzionetsa kwa Iye kuti popanda Iyeyo sungakhale kanthu. Ndiye munthu umapempha chilichonse poti mwini...
by Admin | Nov 7, 2018 | Sunnah
KUKHANZIKIKA NDI KULUNGAMA (Riyaadhu Sswaaliheen “Khomo 8”) Allah Ta’la ananena kuti: فَاسْتَقِمْ كَمَا أُمِرْتَ وَمَن تَابَ مَعَكَ وَلَا تَطْغَوْا إِنَّهُ بِمَا تَعْمَلُونَ بَصِيرٌ “Choncho (E iwe Mtumiki!) Pitiriza kulungama monga momwe...
Your Comments