by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Allah Subhaanah wa Ta’la anatumiza Mneneri Nuh alaih salaam patadutsa zaka 100 pambuyo pa Mneneri Adam alaih salaam. Chiwelengero cha anthu padziko chinachuluka zedi.Panthawiyi, shaytwaan anawasokoneza anthu kotero anali kupembedza mafano, kotero Allah anatumiza...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Pambuyo pa chigumula, anthu a Nuh alaih salaam anachulukana padziko. Mneneri Nuh alaih salaam anali ndi ana komanso zidzulu zambiri, choncho chiwelengero cha anthu padziko chinakula. Ambiri mwa iwo anakhanzikika ku Yemen. Zimakambidwa kuti omwe anakhanzikika kumeneko...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Kalelake kwambiri, Allah Subhannahu wa Ta’la analenga dzuwa, mwezi ndi nthaka. Pambuyo pake anaona kuti zolenga zake sizikukwanira.Choncho anawatuma Angelo ake kuti atenge dothi pa dziko. Angelo aja anamvera ndipo anapititsa dothi kwa Allah lomwe analengera...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Wamva kale mmene Taloot anakumanira ndi asilikali a ku Palestine ndi gulu lake lochepa, ndipo asilikali ake ambiri anathawa ataona gulu la asilikali ambiri a Palestine. Goliat anali mtsogoleri wa asilikali a Palestine ndip anali wamkulu thupi komanso wamphamvu. Iye...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Mneneri Musa alaih salaam anayenda mchipululu usana ndi usiku kulunjika ku Madian, womwe ndi mzinda wapafupi ndi Syria komanso Egypt. Palibe yemwe anali naye paulendowu kupatula Allah Ta’la ndipo chakudya chake chinali mapemphero. Ngakhale anali kumva kutentha...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Musa alaih salaam anakulira m’banja la Chifumu. Mafumu omwe anali kutsogolera dziko la Egypt anali kuchitira nkhanza ana a Ya’qoub alaih salaam, omwe amadziwikanso ndi dzina loti ana a Israel. Iwo anali kugwiritsidwa ntchito nthawi yaitali ndi malipiro...
Your Comments