786…??

786…??

Ambiri mwa ife timakhala tikufunafuna barakah (madalitso) kuchikera mu nambala ya 786 poilemba pamayambiliro pa ma kalata, nkhani, pa grocery komanso malo ambiri. Ena mwaife timailemba nambalayi pa china chane ndikuchikoleka pa galimoto kuti itetezedwe ku ngozi. Ena...
Kuyankhidwa kwa Dua

Kuyankhidwa kwa Dua

“ndipo akakufunsa akapolo anga za ine, ndithu ine ndili pafupi ndimayankha Dua ya opanga dua (kuitana kwa oitana)”  Chisilamu chinalongosola ma condition/zofunika kuti kuti Dua iyankhidwe, komanso chinafotokoza zomwe zimaletsa kuti Dua iyankhidwe. Komanso...
Kuopsa kwa Kumpanga Msilamu Kaafir Popanda Umboni

Kuopsa kwa Kumpanga Msilamu Kaafir Popanda Umboni

 الفتاوى الشرعية في القضايا العصرية #ص٨٢-٨٥ Fatawa Al Shar’iyya fil Qadhaayal ‘Asriya Page 82-85 “Kumuchita munthu kaafir yemwe ali osayenera kumuchita kaafir sizololedwa. Amene akuyenera kumuchita kaafir ndi amene ali oyenera kumuchita kaafir. Amene...
Abale Athu Mchipembedzo

Abale Athu Mchipembedzo

Ngati makolo athu kapena abale athu ali ma kafir, tisawachite kukhala atetezi athu E inu amene mwakhulupirira! Musawachite makolo anu ndi abale anu kukhala atetezi anu ngati (iwo) akukonda kusakhulupirira Mulungu m’malo mokhulupirira (kukhala Asilamu). Ndipo mwa...
Ahlu Bayt…?

Ahlu Bayt…?

HUSSEIN .. MADAD YA HUSSEIN .. YA HUSSEIN !! Nchifukwa chani ma Shia amatamanda ndi kulemekeza Hussein (رضي الله عنه)  yekha ndi kusiya ana ena onse a Ali (رضي الله عنه)? Kodi munayamba mwazifunsapo funso limeneli? Nanga nkhani imeneyi inayamba yakudabwitsanipo?...
Tawbah – Kulapa

Tawbah – Kulapa

Ine ndapanga machimo ambiri  ndipo ndikufuna kubwelera kwa Allah ndikupanga tawba, kulapa koona. Kodi ndingapange bwanji tawbah imeneyi  Tawbah (Kulapa) ndi kokakamizidwa kwa Msilamu aliyense, ngakhaletu kwa makafiri. Munthu aliyense yem,we wafika msinkhu wolembedwa...