Ana Achikazi Ngochititsa Manyazi

Kusiyana kwa pakati pa Baibulo ndi Qur’an pa nkhani ya akazi, kukuyamba pamene mkazi abadwa. Mwachitsanzo, Baibulo limanena kuti nyengo ya kuyera kwa mayi yemwe wabereka mwana wamkazi kumakhala kotalika kawiri kuyerekeza ndi kubadwa kwa mwana wamwamuna (Levitiko...

Cholowa Cha Hawa

Chithunzithunzi chimene Baibulo linaika chokhunza Hawaa, chinapereka maganizo olawika kwambiri kwa amayi mu myambo ya Chiyuda ndi Chikhristu. Anthu ankakhulupilira kuti mayi aliyense anatengera tchimo la mayi Hawaa pa kuphwanya lamulo kwake komanso chinyengo chake...

Kulakwa kwa Hawaa

Zipembedzo zitatuzi zimagwirizana pa mfundo imodzi yofunikira: amayi ndi abambo onse analengedwa ndi Mulungu, Mlengi wa zonse. Komabe, kusagwirizana kumabwera pa kulengedwa kwa munthu woyamba, Adam ndi Hawaa. Ku Chiyuda ndi ku Chikhristu, kulengedwa kwa Adam ndi Hawaa...

Introduction

Five years ago, I read in the Toronto Star issue of July 3, 1990 an article titled “Islam is not alone in patriarchal doctrines”, by Gwynne Dyer. The article described the furious reactions of the participants of a conference on women and power held in...

Mawu Oyamba

Zaka zisanu zapitazo, ndinawerenga m’nyuzipepala ya Toronto Star ya pa July 3, 1990, nkhani yoti “Chisilamu sichili chokha mu ulamuliro wa amuna (patriarchal Doctrine)”, yolembedwa ndi Gwynne Dyer 1. Mlembi anafotoko munkhaniyi za momwe anthu...

Nthawi za Mapemphero

Ambiri masiku ano amasokonezeka nthawi ya swalat yomwe anaphunzitsa Mtumiki salla Alaih waallam, ndi  wotchi makamaka akapita dziko lina. Ena anati “mzikiti womwe timaswali kuno ndi wa Mashia chifukwa akumachita adhaan ya Dhuhr past 1, pomwe ku Malawi...