Kulemekeza ma Sheikh

Ma Ulamaa (anthu ozindikira komanso amaphunzitsa za deen ya Chisilamu), ndi anthu olemekezeka pamaso pa Allah chifukwa choti iwo ndi Alowammalo a Aneneri, ndi atsogoleri oyenera kuwalemekeza kuposa mtsogoleri wa dziko chifukwa akutitsogolera ku moyo wosatha....
Mkazi Kuvala Buluku

Mkazi Kuvala Buluku

“Ndi zoletsedwa mu Chisilamu mkazi kuvala buluku (thalauza) lothina ndikuonetsa mmene thupi lake liliri. Ndipo chilango chake ndi choopsa zedi chifukwa mchitidwe umenewu umafalitsa machimo pa dziko.” Darul Iftail Misriy Allah anaika ndondomeko ya momwe...

Mzimai Kuzola Zonunkhira (Perfume)

Mtumiki salla Allah alaih wasallam analangidza Asilamu kuti likafika tsiku la Chisanu adzidzikongoletsa posamba,  kuwenga zikhadabo,  kusamalira tsitsi,  Kuala zovala zokongola, kudzola zonunkhiritsa ndi zina zotero. Swalat ya Jum’ah ndi fardh kwa Msilamu...

Kunyoza ma Sheikh

Munthu wina aliyense zimatengedwa zoyankhula zake kapena kusiyidwa, kupatula Mtumiki Muhammad salla Allah alaih wasallam, zoyankhula zake sitimayenera kudzisiya. Aalim wina aliyense ali ndi ilm yomwe ili ndi zoona komanso zabodza, zabwino komanso zolakwika. Choncho...

A Sheikh Refused Advice From His Students

Is it permissible for an Islamic teacher who has students (males & females) for him to inform his students that he does not want any advises? It could be that what led this teacher to say such a thing is the misconduct of some students who advised him in an...