by Admin | Oct 27, 2018 | Fatawa
Funso: Abale anga okondedwa Mchipembedzo ndifunse nawo; kodi mwana ndibwino kumpatsa dzina lakuti “Mashaallah”? Ena akuti ndi zotheka chifukwa pali monga “Shukuran”, kuchokera ku Shukru-Llaah”, choncho “Mashaa-Allah”...
by Admin | Oct 27, 2018 | Fatawa
Kuchokera mu buku: “Ighaathatu Llahafaan min Maswaaid Shaytan” Lolembedwa ndi Ibn AlQayyim AlJawziy Nkhani ya nyimbo inali yomveka kalekale pamene kunalibe zomwe zikuchitika masiku ano. Ngakhale zili zomveka kuti nyimbo zogwiritsa ntchito zida ndi haraam, mpovuta kuti...
by Admin | Oct 6, 2018 | Fatawa
Mkazi ndiwololedwa kugwira ntchito. Koma pali zingapo zofunika kutsatira komanso zina zofunika kupewa. Pachiyambi penipeni, tiona shari’ah, ndipo tisiye zomwe society imafuna. Mkazi ndimunthu amene amayenera kukhala panyumba, kusamalira m’nyumba, ana...
by Admin | Oct 6, 2018 | Fatawa
الاعتقاد أننا سننادى بأسماء أمهاتنا يوم القيامة Chikhulupiliro choti tikaitanidwa ndi maina a mayi athu tsiku la Qiyamah Ma sheikh ena amalalikira ndikuphunzitsa anthu kuti tsiku la Qiyaamah akuti tizikaitanidwa ndi a maina amayi athu osati ndi maina abambo athu;...
by Ummah | Jun 5, 2018 | Fatawa
Is this a major sin, a minor sin, or does it even make you a disbeliever when you fail to make up the missed days of fasting until the next Ramadan starts? Answer All perfect praise be to Allah, The Lord of the worlds. I testify that there is none worthy of worship...
by Ummah | Jun 5, 2018 | Fatawa
I only recently accepted Islam into my life, but I was raised as a Christian. As a result, I own many things that are haram, especially things carrying images. There are many charity organizations around me that ask for such things, because I live in a non-Muslim...
Your Comments