by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Sulaiman analowa ufumu pambuyo pa imfa ya Dawud alaih salaam ndipo anapempha Allah kuti ampatse ufumu womwe sanayambe wapatsidwa wina aliyense mbuyomo. Allah anampatsa zofuna zake pamodzi ndi zina zambiri, monga kutha kuilamula mphepo, komanso anali kumva zilankhulo...
by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Ubwino wa Isa alaih salaam ukuwonekera kuchokera mu ntchito yomwe anapatsidwa. Anali Mneneri omalidza asanabwere Mneneri Muhammad salla Allah alaih wasallam, komanso anali Mtumiki omaliza kwa ana a Israel. Allah analipatula banja la Isa alaih salaam ndi madalitso,...
Your Comments