by Hamdan Zefa | May 22, 2022 | Featured, Shia
Kutamandidwa konse ndi kwa Allaah, Wapamwambamwamba, Yemwe alibe wothandizana naye mu Ufumu Wake, Yemwe ali m’Modzi, Yemwe ali Wakutha kuchita chili chonse ndipo kwa Iye ndi komwe kuli Chiongoko. Mtendere ndi madalitso zipite kwa Mtumiki Muhammad (ﷺ), aku banja ake...
by Admin | May 22, 2022 | Featured, Shia
Bodza la Mashia lonena kuti pali umboni woti Ali radhia Allahu anhu ndi Khalifa woyamba osati Abu Bakr radhia Allahu anhu 185- حتى لا ننخدع حقيقة الشيعة Pamene ma Swahaba wonse anagwirizana za utsogoleri komanso ulowammalo wa Abu Bakr, ‘Umar, ‘Uthman, kenako Ali...
by Admin | May 22, 2022 | Featured, Shia
Idris Al Maghribi anali Msilamu waku Morocco ndipo atakumana ndi da’wah ya ma Shia, anaganiza zosiya Chisilamu nkulowa Shia. Pa mwambo wa “kusinguka” (kutuluka mu chipembedzo china kuliwa mu chipembedzi china), pamene Yaasir Al Habib yemwe ndi mmodzi...
by Admin | May 22, 2022 | Featured, Shia
1. Chiphunzitso cha chi Shia chimanena kuti “Aah” ndilimodzi mwa maina a Allah. Umboni: Ma’anil Akhbaar, chitabu cholembedwa ndi Al Qummi, page 304: Onani chithunzi 2. Ma Shia amakhulupilira kuti Abu Talib (Malume a Mtumiki), Abdullah ndi Aaminah (Makolo a...
Your Comments