by Admin | May 6, 2020 | Fasting, Featured, Fiqh
Anzathu ena ambiri akamapanga wudhu sachukucha mkamwa akuti kuwopa kuwononga swaum yawo. Zimenezitu ndizolakwika pazifukwa zambiri: 1. Kuchukucha mkamwa sikuwononga swaum ngati ukupanga wudhu, ngakhale madzi atalowa kukhosi mwangozi swaum yako sinawonongeke. 2. Palibe...
Your Comments