by Admin | Nov 13, 2018 | Fiqh
Ndi chifukwa chani timayenera kutsuka ndi mchenga kamodzi? “Kuyeretsa kwa chiwiya chanu chomwe wanyambitamo galu ndi kutsuka ka 7, kamodzi kakeko ndi mchenga”. Tonse tikudziwa kuti Mtumiki anatiuza kuti tidzitsuka chiwiya chomwe galu wanyambita ka seven,...
Your Comments