by Admin | Jul 17, 2020 | Islam, Islamic Manners
Pali anthu ena anazolowera kulumbira m’Dzina la Allah, mwachitsanzo kunena kuti “Wallahi…”, ndipo amachitenga kukhala chizolowezi chawo pakuyankhula kulikonse, zofunikira ngakhale zosafunikira. Chizolowezi choterechi ndicholakwika kwambiri....
Your Comments