by Admin | May 6, 2020 | Fasting, Featured, Fiqh
Anzathu ena ambiri akamapanga wudhu sachukucha mkamwa akuti kuwopa kuwononga swaum yawo. Zimenezitu ndizolakwika pazifukwa zambiri: 1. Kuchukucha mkamwa sikuwononga swaum ngati ukupanga wudhu, ngakhale madzi atalowa kukhosi mwangozi swaum yako sinawonongeke. 2. Palibe...
by Admin | Jun 8, 2019 | Fasting
Malamulo Ochititsa kuti Munthu Asale – Chisilamu: Yemwe sali Msilamu sanalamulidwe kusala – Nzeru: Wamisala sanalamulidwe kusala – Kutha Msinkhu: Mwana wamng’ono sanalamulidwe, koma ngati angakwanitse kusala alamulidwe kutero kuti...
by Admin | May 15, 2019 | Fasting
Timamva kuti shaytwaan amamangidwa mwezi wa Ramadhan, kodi ruqya yochotsa ziwanda ndiyololedwa kupanga mwezi wa Ramadhan? Ngati zili zololedwa, ziwanda zingapezeke bwanji? Ruqya ndiyololedwa kupanga nthawi iriyonse, tsiku lirilonse komanso mwezi uliwonse. Palibe...
by Admin | May 15, 2019 | Fasting
أعوذ بالله من الشيطان الرجيم بسم الله الرحمن الرحيم الحمد لله رب العالمين رب كل شيئ ومالكه وسع كل شيئ علما، والصلاة والسلام على سيد صاحب الشرف من المرسلين وآله وأصحابه وتابعيه وجميع من اهتدى بهديه إلى يوم الحشر أما بعد يقول الله تعالى وَلاَ تَقْرَبُواْ الزِّنَى...
Your Comments