by Admin | Nov 20, 2019 | Islam
Maloto amachitika pamene munthu wagona tulo ndipo mzimu wake umachoka mthupi ndikupita kwina kumene atha kukakumana ndi mizimu ya anthu ena, omwalira kapena amoyo omwe ali mtulo ngati iyeyo. Choncho Allah amangosiya connection pakati pa thupi ndi mzimu wake, ndipo...
by Admin | Nov 7, 2018 | Islam, Sunnah
Funso Loyamba: Assalaam Alaykum Shekhy! Kodi ndi zizindikiro zanji zomwe amaonetsa mwana wamng’ono pomwe walozedwa ndiye wawelengeredwa ma Aayat a Ruqya; tingadziwe bwanji kuti ufitiwo watha? Funso Lachiwiri: Kodi mwana wamng’ono oti sayankhula ndiye...
Your Comments