by Kuunikira | May 23, 2022 | Featured, Kuunikira
“Akalowa bwanji ku ng’anjo ya moto akadaulo, akatswiri komanso anthu ena amene anachita ndi kugwira ntchito zopambana, ndizopititsa patsogolo umoyo wa anthu pa dziko lino lapansi?. – Anthu okanira amene anagwira ntchito yotamandika pa dziko lapansi,...
by Admin | Jan 13, 2020 | Fatawa
Funso: Kodi ndichifukwa chani akazi wa Chisilamu tikamawafunsira amanyada kwambiri ndipo akakulola amapanga zamwano zoyelekedwa, ndye tikamakwatira achikunja ndikulakwa ?? Yankho: Allah Ta’la akunena mu Qur’an kuti: وَمَا كَانَ لِمُؤْمِنٍ وَلَا مُؤْمِنَةٍ...
Your Comments