by Admin | Sep 4, 2021 | Featured, Islam, Misconceptions
Kuchokera mu Minhaajul Qaaswideen fi Fadhlil Khulafaai Rraashideen page 187, tidziwa kuti nawo ma Khawaarij amadana ndi ena mwa ma Swahaba. Khawaarij ndigulu la anthu omwe anali limodzi ndi Ali radhia Allah anhu pa nkhondo zake, koma anamutuluka ndikumuwukira pamene...
Your Comments