by Admin | Jan 13, 2020 | Fatawa
بسم الله الرحمن الرحيم ٱلْيَوْمَ أُحِلَّ لَكُمُ ٱلطَّيِّبَٰتُۖ وَطَعَامُ ٱلَّذِينَ أُوتُوا۟ ٱلْكِتَٰبَ حِلٌّ لَّكُمْ وَطَعَامُكُمْ حِلٌّ لَّهُمْۖ وَٱلْمُحْصَنَٰتُ مِنَ ٱلْمُؤْمِنَٰتِ وَٱلْمُحْصَنَٰتُ مِنَ ٱلَّذِينَ أُوتُوا۟ ٱلْكِتَٰبَ مِن قَبْلِكُمْ إِذَآ...
by Admin | Jul 2, 2019 | Fatawa
Funso: Ena chifukwa cha kuopa kukhala osakwatira kapena osakwatiwa, mapeto ake amakwatira munjira yosakhala bwino kapenanso kukwatira mkazi/mwamuna yemwe amanena kuti “zimenezo (myambo ya Chisilamu) ine sindingakwanitse” koma iwe ukumukwatirabe poopa kuti...
by Admin | Jul 2, 2019 | Fatawa
Anthu anaika freedom of choice pa kukwatira ndikukhala pa banja lovomerezeka, chifukwa chopangidwa influence ndi ma ideologies a ku west omwe adadza kudzalimbana ndi malamulo a Deen ya Chislamu, omwe amatsutsa kalikonse ponena kuti Chisilamu chimapondereza ufulu wa...
by Admin | Jul 2, 2019 | Fatawa
Gawo Loyamba: Banja ndi chinthu chofunika kuchikhonzekera pambuyo pa imfa pamoyo wadziko lapansi, chifukwa banja: 1. Limakulowetsa mu chikhalidwe chatsopano chomwe umalidzire nacho moyo wapadziko. 2. Komanso banja ndi chinthu chomwe chimamukwaniritsira munthu half ina...
by Admin | Jun 9, 2019 | Marriage
Qur’an Yolemekezeka yatchula munthu mmodzimmodzi momveka bwino, omwe omwe sali oyenera kumanga nawo banja. Anthu amenewa ndi awa: حُرِّمَتْ عَلَيْكُمْ أُمَّهَاتُكُمْ وَبَنَاتُكُمْ وَأَخَوَاتُكُمْ وَعَمَّاتُكُمْ وَخَالاَتُكُمْ وَبَنَاتُ الأَخِ وَبَنَاتُ الأُخْتِ...
Your Comments