by Admin | Feb 16, 2020 | Featured, Sunnah
Pali ma hadith omwe anapekedwa nalembedwa mu buku kuti tidziwerenga poikira umboni kuti kuwerenga Qur’an ku Manda ndi Sunnah. Ma hadith amenewa ndi osafunika kuti tidziwagwiritsa ntchito tikawaona. Chifukwa ndi ma hadith oipa omwe amanamizira Mtumiki salla Allah...
by Admin | Oct 10, 2018 | Islam
Nkhani inachokera kwa al-Bara’ ibn ‘Aazib yemwe anati: “tinapita ndi Mtumiki (Mtendere ndi Madalitso zipite kwa Iye) kumwambo woika mmanda mmodzi wa ma Ansar (mzika ya mumzinda wa Madina), ndipo titafika pa manda, tinapeza kuti sadaikidwe ku mphanga la manda. Kenako...
Your Comments