by Admin | Feb 27, 2022 | Featured, Islam, Sunnah
Kodi n’chifukwa chani ma Sheikh amalalikira pamaliro ndi kumanda pomwe imfayo payokha ndi mlaliki? Tibwelere kaye mbuyo pang’ono, makamaka pa mawu oti: كَفَى بِالمَوْتِ وَاعِظًا “Yakwanira imfa kukhala mlaliki” Mawu amenewa ambiri amanena kuti ndi Hadith ya...
by Admin | Jul 18, 2020 | Fiqh, Islam
1. Imaam kupanga dua ya pagulu pambuyo pa swalat Janaazah. Palibe chiphunzitso choti imaam akaswalitsa swalat Janaazah apange dua anthu nkumavomera kuti Ameen. 2. Kuimba kapena kupanga ma adhkaar mokweza poperekeza kumanda Imeneyi si sunnah ya Mtumiki ndi...
by Admin | Nov 11, 2019 | Featured, Salaat
Tiyeni titsegule page103 ya chitabu cha أحكام الجنائز وبدعها cha Allaamatu Sheikh Muhammad Naasirul-Deen Al Albaaniy, ndipo tiyambire pa mutu wa number 13 kumapita kutsogolo mmapage otsatira mu chitabuchi Zoyenera kuchita pa Janaaza Janaaza ndi mwambo wa maliro womwe...
Your Comments