by Admin | Nov 19, 2018 | Islam
Ngati makolo athu kapena abale athu ali ma kafir, tisawachite kukhala atetezi athu E inu amene mwakhulupirira! Musawachite makolo anu ndi abale anu kukhala atetezi anu ngati (iwo) akukonda kusakhulupirira Mulungu m’malo mokhulupirira (kukhala Asilamu). Ndipo mwa...
Your Comments