by Admin | May 6, 2019 | Islam
Nthawi zambiri timakhala tikulimbikira kuchenjeza za bid’ah chifukwa ndi chinthu choopsa mu deen kuposa kuchita tchimo. Msilamu aliyense akuyenera kuidziwa bid’ah mokwanira kuti aipewe. Komanso monga momwe tikudziwira, cholinga chathu chachikulu ndi...
by Admin | Nov 9, 2018 | Islam
Ine ndapanga machimo ambiri ndipo ndikufuna kubwelera kwa Allah ndikupanga tawba, kulapa koona. Kodi ndingapange bwanji tawbah imeneyi Tawbah (Kulapa) ndi kokakamizidwa kwa Msilamu aliyense, ngakhaletu kwa makafiri. Munthu aliyense yem,we wafika msinkhu wolembedwa...
Your Comments