by Admin | Oct 27, 2018 | Fatawa
Kuchokera mu buku: “Ighaathatu Llahafaan min Maswaaid Shaytan” Lolembedwa ndi Ibn AlQayyim AlJawziy Nkhani ya nyimbo inali yomveka kalekale pamene kunalibe zomwe zikuchitika masiku ano. Ngakhale zili zomveka kuti nyimbo zogwiritsa ntchito zida ndi haraam, mpovuta kuti...
by Admin | Oct 24, 2018 | Sunnah
Ena Mwa Maina Ololedwa Kuwapatsa Ana Athu Maina a Chimuna Abdul+(Dzina lirilonse la Allah) Abu-Bakr Adam Ahmad Akram Al Ameen Ali Ayyub Daud Dhakiyyu Dhul Kifl Farhan Fauzi Haaritha Haashir Harun Hassan Hud Hudhaifa Hussein Ibrahim Idris Ilyaas Isa Is’haaq...
by Admin | Oct 24, 2018 | Sunnah
“Maina oletsedwa Kuwapatsa Ana Athu” zitsanzo za maina abwino Maina oyenera kuwapatsa ana athu MCHISILAMU akuyenera kukhala omwe ali abwino, KUPATULA awa: 1. Maina omwe ali ndi liwu la Ibaadah “Abdul-” kumayambiliro, nkulumikizidwa ndi maina...
Your Comments