by Admin | Dec 19, 2018 | Islam
“ndipo akakufunsa akapolo anga za ine, ndithu ine ndili pafupi ndimayankha Dua ya opanga dua (kuitana kwa oitana)” Chisilamu chinalongosola ma condition/zofunika kuti kuti Dua iyankhidwe, komanso chinafotokoza zomwe zimaletsa kuti Dua iyankhidwe. Komanso...
by Admin | Nov 8, 2018 | Islam
Kodi Istikhaarah ndi chani? Istikhaarah mu chiyankhulo cha Arabic Kumeneku ndi kupempha kusankha kwabwino pa chinthu. Amanena kuti: “pempha chisankho kwa Allah ﷻ , akusankhira”. Istikhaarah mu Deen Kupempha kusankha, kapena kuti kupempha kuti akuchotsere...
Your Comments