by Admin | Jul 26, 2020 | Fatawa, Featured, Islam
Mafunso omwe timafunsa pa za deen timafuna kudziwa kuti kodi deen yathu tiyendetse bwanji. Timafuna kudziwa kuti kodi ibaada tingachite bwanji, nanga chikhulupiliro chathu tingachisamale bwanji. Kudzera mu kufuna kudziwa zinthu momwemo, ambiri tili ndi chizolowezi...
Your Comments