by Kuunikira | May 24, 2022 | Featured, Kuunikira
Pakukhala kuti Chisilamu chidaunikira mbali zonse za umoyo, Mu Qur’an ndi Mahadith (zoyankhula za mtumiki). Ndipo masahabah Adagwira ntchito yotamandika yotulutsa khokwe za maphunziro kuchokera mu Qur’an ndi Mahadith, pambuyo pawo padabweraso Ma Imam ndi...
by Admin | Aug 7, 2019 | Featured
Zipembedzo zitatuzi zili ndi chikhulupiliro chosagwedezeka pa kufunikira kwa ukwati ndi banja. Ndipo zimavomerezana pa utsogoleri wa mwamuna pa banja. Komabe, pali kusiyana kwakukulu pakati pa zipembedzozi, pa malire a utsogoleri umenewu. Chikhalidwe cha Chiyuda ndi...
Your Comments