by Admin | Jun 28, 2019 | Prophets
Ubwino wa Isa alaih salaam ukuwonekera kuchokera mu ntchito yomwe anapatsidwa. Anali Mneneri omalidza asanabwere Mneneri Muhammad salla Allah alaih wasallam, komanso anali Mtumiki omaliza kwa ana a Israel. Allah analipatula banja la Isa alaih salaam ndi madalitso,...
by Admin | Dec 19, 2018 | Islam
“ndipo akakufunsa akapolo anga za ine, ndithu ine ndili pafupi ndimayankha Dua ya opanga dua (kuitana kwa oitana)” Chisilamu chinalongosola ma condition/zofunika kuti kuti Dua iyankhidwe, komanso chinafotokoza zomwe zimaletsa kuti Dua iyankhidwe. Komanso...
Your Comments