by Admin | Jan 18, 2019 | Islam
Funso: “Mwamuna achoke muchipembedzo chake cha Chisilamu mkumtsatira muchipembedzo chake (ndikhulupilira mukutanthauza kumtsatira mkazi). Ndafunsa funsoli chifukwa ndakhala ndikuona ambiri kuno ku Joni akupanga zimenezo akuti chifukwa chofuna kukhala mwa...
by Admin | Oct 6, 2018 | Islam
Imaan – الإيمان Imaan (chikhulupiliro) yeniyeni sichinthu chophweka kuchipeza. Imaan yomwe sivuta kuipeza ndi imene imapezeka kudzera mu nkhani zopeka. Munthu akhonza kukhala ndi imaan pa zinthu zabodza ndikumalimbikira ibaadah yake, koma kuchokera mu...
Your Comments