by Admin | Oct 27, 2018 | Sunnah
Kodi kumuona mkazi ndizololedwa usanapange naye nikkah? Ndizololedwa kumuona mkazi yemwe wamufunsira ndipo mwatsimikiza kuti mukwatirana. Malamulo a Chisilamu akunkera navutatuvabe poti anthufe tachulutsa kuyendera zomwe zimatisangalatsa osati zomwe Shariah imalola....
by Admin | Oct 27, 2018 | Fatawa
Kuchokera mu buku: “Ighaathatu Llahafaan min Maswaaid Shaytan” Lolembedwa ndi Ibn AlQayyim AlJawziy Nkhani ya nyimbo inali yomveka kalekale pamene kunalibe zomwe zikuchitika masiku ano. Ngakhale zili zomveka kuti nyimbo zogwiritsa ntchito zida ndi haraam, mpovuta kuti...
by Admin | Oct 24, 2018 | Sunnah
“Maina oletsedwa Kuwapatsa Ana Athu” zitsanzo za maina abwino Maina oyenera kuwapatsa ana athu MCHISILAMU akuyenera kukhala omwe ali abwino, KUPATULA awa: 1. Maina omwe ali ndi liwu la Ibaadah “Abdul-” kumayambiliro, nkulumikizidwa ndi maina...
Your Comments