by Admin | Apr 6, 2021 | Fatawa, Featured, Islamic Manners
Basharul Haafi rahimahu Allah anati: “Yemwe amakonda kuti azifunsidwa (za deen), sali oyenera kufunsidwa” قال بشر الحافي رحمه الله تعالى: مَن أحبَّ أن يُسْأَلَ، فَليسَ بِأَهْلٍ لِأَنْ يُسْألَ. Mau awa ndi akuya zedi. Allah atipatse kumvesetsa Phunziro:...
by Admin | Jul 26, 2020 | Fatawa, Featured, Islam
Mafunso omwe timafunsa pa za deen timafuna kudziwa kuti kodi deen yathu tiyendetse bwanji. Timafuna kudziwa kuti kodi ibaada tingachite bwanji, nanga chikhulupiliro chathu tingachisamale bwanji. Kudzera mu kufuna kudziwa zinthu momwemo, ambiri tili ndi chizolowezi...
by Admin | Jul 13, 2019 | Fiqh
The process of Fatwa: Fatwa is a very sensitive matter and has a great status in Islam. Allah says (what means): “They ask you about the sacred month – about fighting therein…” [Qur’an 2:217]. Allah also says (what means): “They request from you a...
by Admin | May 5, 2019 | Fatawa
Anthu ena amaganiza kuti Da’wah (kuitanira kwa Allah) palibe yemwe angapange kupatula ma ulamaa okhaokha, ndipo omwe akuphunzira kwa ma Ulamaawo sakukakamizidwa kupanga Da’wah. Mutithandiza bwanji pa zimenezi? Sikuti ndi maganizo chabe, koma ndizoona....
by Admin | Jan 24, 2019 | Islam
Kugwiritsa Maphunziro Pakati Pa Achichepere” Kuchokera mu “Al Kabeer wal Awsat” ya Al Tabarani, anati kuchokera kwa Abi Umaya Al Jumahi radhia Allah anhu: “إن من أشراط الساعة – وفي رواية: ثلاثاً: إحداهن – أن يُلتمس العلم عند...
Your Comments