by Admin | Jul 26, 2020 | Fatawa, Featured, Islam
Mafunso omwe timafunsa pa za deen timafuna kudziwa kuti kodi deen yathu tiyendetse bwanji. Timafuna kudziwa kuti kodi ibaada tingachite bwanji, nanga chikhulupiliro chathu tingachisamale bwanji. Kudzera mu kufuna kudziwa zinthu momwemo, ambiri tili ndi chizolowezi...
by Admin | May 5, 2019 | Fatawa
Anthu ena amaganiza kuti Da’wah (kuitanira kwa Allah) palibe yemwe angapange kupatula ma ulamaa okhaokha, ndipo omwe akuphunzira kwa ma Ulamaawo sakukakamizidwa kupanga Da’wah. Mutithandiza bwanji pa zimenezi? Sikuti ndi maganizo chabe, koma ndizoona....
by Admin | Jan 11, 2019 | Fatawa
Kutulutsa zinthu za mu Mzikiti Sizololedwa kutulutsa zinthu za mu mzikiti kukadzigwiritsira ntchito malo ena osakhala munzikiti momwemo. Kubwereka mkeka, kapena Qur’an kaya mabuku aliwonse komanso china chirichonse chomwe chinaikidwa mu mzikiti kuti...
by Admin | Dec 2, 2018 | Islam
الفتاوى الشرعية في القضايا العصرية #ص٨٢-٨٥ Fatawa Al Shar’iyya fil Qadhaayal ‘Asriya Page 82-85 “Kumuchita munthu kaafir yemwe ali osayenera kumuchita kaafir sizololedwa. Amene akuyenera kumuchita kaafir ndi amene ali oyenera kumuchita kaafir. Amene...
Your Comments