by Admin | Mar 28, 2022 | Fasting, Fatawa, Featured, Fiqh
يجب صيام رمضان عن طريقتين فقط: إما١- عن طريق رؤية هلال رمضان. أو٢- عن طريق اتمام شعبان ثلاثين يوما. Kuyamba kusala mwezi wa Ramadhan kukuyenera kuchitika munjira ziwiri izi:1. Mukawuona mwezi wa Ramadhan. Kapena2. Mwezi wa Sha’baan ukakwanira masiku 30. قال...
by Admin | Mar 18, 2022 | Fasting, Fatawa, Featured, Fiqh, Islam
Kodi ndichiphunzitso cha Mtumiki kusala kwa tsiku la 15 Sha’baan? Hadith yomwe yabwera polimbikitsa swalaat ndi kusala komanso kuchita ibaada yosiyanasiyana pa 15 Sha’baan, siili mugulu la ma Hadith ofooka (a dhwaeef) koma ili mugulu la ma Hadith opeka komanso abodza...
by Admin | Sep 4, 2021 | Fasting, Featured, Fiqh, Islam, Sunnah
Kuchokera m’mawu omwe anthu amati ndi ochokera kwa Mtumiki salla Allah alaih wasallam, عن أبي هريرة قال: قال رسول الله ﷺ : أول شهر رمضان رحمة، وأوسطه مغفرة، وآخره عتق من النار. منكر، روه الديلمي Nkhani inachokera kwa Abi Hurairah radhia Allah anhu, anati:...
by Admin | Apr 8, 2021 | Fasting, Featured, Fiqh
Kuyambikidwa konse nkwa Allah Mwini zolengedwa zonse, Mtendere ndi Madalitso zipite kwa Mtumiki wake wolemekezeka. Kodi tikhonzekere motani mwezi wa Ramadhan? Pamene tili pa chitseko cha mwezi wa Ramadhan, aliyense mwa ife akuyenera kuti akudziwa komwe akupita...
by Admin | Jun 8, 2019 | Fasting
Malamulo Ochititsa kuti Munthu Asale – Chisilamu: Yemwe sali Msilamu sanalamulidwe kusala – Nzeru: Wamisala sanalamulidwe kusala – Kutha Msinkhu: Mwana wamng’ono sanalamulidwe, koma ngati angakwanitse kusala alamulidwe kutero kuti...
Your Comments