by Admin | May 2, 2019 | Islam
Kusintha dzina la bambo ndikutenga la mwamuna wake pambuyo pa kukwatiwa Mkazi kusintha dzina labambo ake ndikutenga la munthu wina wake ndi kulakwa kwakulu. Dzina la bambo limalongosola chibale cha kobadwira (lineage),, tsopano mkazi akasintha dzina la bambo ake...
by Admin | Oct 27, 2018 | Fatawa
Funso: Abale anga okondedwa Mchipembedzo ndifunse nawo; kodi mwana ndibwino kumpatsa dzina lakuti “Mashaallah”? Ena akuti ndi zotheka chifukwa pali monga “Shukuran”, kuchokera ku Shukru-Llaah”, choncho “Mashaa-Allah”...
by Admin | Oct 24, 2018 | Sunnah
Ena Mwa Maina Ololedwa Kuwapatsa Ana Athu Maina a Chimuna Abdul+(Dzina lirilonse la Allah) Abu-Bakr Adam Ahmad Akram Al Ameen Ali Ayyub Daud Dhakiyyu Dhul Kifl Farhan Fauzi Haaritha Haashir Harun Hassan Hud Hudhaifa Hussein Ibrahim Idris Ilyaas Isa Is’haaq...
by Admin | Oct 24, 2018 | Sunnah
“Maina oletsedwa Kuwapatsa Ana Athu” zitsanzo za maina abwino Maina oyenera kuwapatsa ana athu MCHISILAMU akuyenera kukhala omwe ali abwino, KUPATULA awa: 1. Maina omwe ali ndi liwu la Ibaadah “Abdul-” kumayambiliro, nkulumikizidwa ndi maina...
Your Comments