by Admin | Dec 10, 2020 | Featured, Islam
Kuchokera kwa Ibn Abbas radhia Allah anhu: Mtumiki wa Allah (ﷺ) amatuluka mnyumba mwa mkazi wake, Juwayriyyah – dzina lake koyamba linali Barrah, koma anasintha – pamene Mtumiki anatuluka, Juwayriyyah anali pamalo opemphelera mpaka pamene anabwelera....
Your Comments