by Admin | Jul 31, 2019 | Featured
Chiwerewere ndi tchimo muzipembedzo zonse. Baibulo linaika chilango cha imfa kwa wachiwerewere wamwamuna ndi wamkazi (Levitiko 20:10). Chisilamu chimalanganso chimodzimodzi wachiwerewere wa mwamuna ndi wamkazi (24: 2). Komatu ngakhale zili choncho, tanthauzo la...
Your Comments