by Admin | Oct 10, 2018 | Islam
Nkhani inachokera kwa al-Bara’ ibn ‘Aazib yemwe anati: “tinapita ndi Mtumiki (Mtendere ndi Madalitso zipite kwa Iye) kumwambo woika mmanda mmodzi wa ma Ansar (mzika ya mumzinda wa Madina), ndipo titafika pa manda, tinapeza kuti sadaikidwe ku mphanga la manda. Kenako...
Your Comments